Home Chichewa MACOKASA LATI ANTHU ONSE OYENDETSA NJINGA ZAMOTO ATATSATIRA MALAMULO

MACOKASA LATI ANTHU ONSE OYENDETSA NJINGA ZAMOTO ATATSATIRA MALAMULO

by Andre Harare
0 comments

Bungwe la MACOKASA lati anthu onse oyendetsa njinga zamoto atatsatira ndondomeko yomwe boma layamba  pa kalembera wa ziphaso za njinga zamoto ndi zoyendetsela zithandiza kuchepetsa ngozi zapamseu ndi upandu mudziko muno.

Wapampando wa bungwe la  MACOKASA, Moses Mwalabu wayankhula izi ku pa msika wa Kamwendo ku Mchinji pamsokhano wowadziwitsa anthu za ndondomekoyi.

Ndondomeko ya Kulembetsa kwa njinga zamoto ndi kupereka ziphaso lomwe limazike pa June 30, 2025 ithandiza oyendetsa njinga zamoto kukhala ndi chitetezo chokwanira.

Iwo ati aliyense amene alephere kutsatira kalembera wa njinga zamoto womwe ukuchitika adzalandira chilango.

Iwo ati akuyembekezera kuti oyendetsa njinga zamoto okwana 5 Million akhala maembala abugwe la MACOKASA

Wapampando wapolisi ya mudzi ya pakwamwendo a Ishmael Mdoka wati kalemberayo uthandiza oyendetsa njinga zamoto kutsatira malamulo apamseu ndikuchepetsa ngozi za pamseu..

You may also like

Leave a Comment

Mudziwathu Community Radio Station was established in 2006 with funding from the American Institute for Research and Radio Systems Inc. It is licensed by the Malawi Regulatory Authority to serve communities in Mchinji District and surrounding areas, broadcasting on a frequency of 107.6 FM. The station’s mission is to promote socio-economic development within the district. Key focus areas include agriculture, health, gender equality, women’s empowerment, and youth development.

Newsletter

Subscribe my Newsletter for new blog posts, tips & new photos. Let's stay updated!

@2025 – All Right Reserved. MACRA Community Radios

Are you sure want to unlock this post?
Unlock left : 0
Are you sure want to cancel subscription?
-
00:00
00:00
Update Required Flash plugin
-
00:00
00:00