Home Chichewa ADINDO APEMPHA ANTHU KU MCHINJI KUTSATIRA MALAMULO OTETEZA MAUFULU A ANA.

ADINDO APEMPHA ANTHU KU MCHINJI KUTSATIRA MALAMULO OTETEZA MAUFULU A ANA.

by Vester Chunga
0 comments

Wolemba: Vester Chunga

Mkulu wa bwalo loweruza milandu  m’bomali , A  Fred Juma Chilowetsa anati ngati anthu azitsatira malamulo oteteza ana ziwapangitsa kusiya kuchitira nkhanza ana komanso ana  adzilandira chithandizo choyenera ngati achitiridwa nkhaza.

Iwo anati dziko la Malawi likuyenera kuti linakwanilitse kukhazikitsa  ndondomeko zonse zomwe zili muli lamulo loteteza la ana la Child Care and protection justice act kuti ana asiye makhalidwe a kuba ndi upandu.

Izi zanenedwa lolemba, pamsokhano omwe bugwe la Girls Activists Youth organization ( GAYO) linachititsa pa bwalo lazamasewero  la sukulu yapulayimale ya Chakhanga kwa mfumu yayikulu Kapondo ,m`bomali okhudza malamulo ndi chitetezo cha ana.

Isabelo Jere , Woona za ma pologalamu ku bugwe la Girls Activists youth organization wapepha adindo m`madera kuti akuyenera kukhazikitsa  magulu oyang`anira  chitetezo cha ana komanso kukhala patsogolo  kuphunzitsa anthu za ubwino oteteza ana ndi kutsatira malamulo.

You may also like

Leave a Comment

Mudziwathu Community Radio Station was established in 2006 with funding from the American Institute for Research and Radio Systems Inc. It is licensed by the Malawi Regulatory Authority to serve communities in Mchinji District and surrounding areas, broadcasting on a frequency of 107.6 FM. The station’s mission is to promote socio-economic development within the district. Key focus areas include agriculture, health, gender equality, women’s empowerment, and youth development.

Newsletter

Subscribe my Newsletter for new blog posts, tips & new photos. Let's stay updated!

@2025 – All Right Reserved. MACRA Community Radios

Are you sure want to unlock this post?
Unlock left : 0
Are you sure want to cancel subscription?
-
00:00
00:00
Update Required Flash plugin
-
00:00
00:00