Home Chichewa MABUGWE OMWE SIABOMA KU MCHINJI ATI NDIKOFUNIKA KUTI ANTHU ADZITENGA NAWO GAWO

MABUGWE OMWE SIABOMA KU MCHINJI ATI NDIKOFUNIKA KUTI ANTHU ADZITENGA NAWO GAWO

by Andre Harare
0 comments

Mabugwe omwe siaboma m`boma la mchinji ati ndikofunika kuti anthu adzitenga nawo gawo pakuyendetsedwe  kazitukuko zomwe zikuchitika m`bomali

Malingana ndi wachiwiri Wamkulu wabungwe omwe siaboma m`bomali aDavis Damson, wati nzika zomwe ziyenerera kupindula pazitukuko  ngati zitenga nawo gawo pakayendetsedwe kazitukuko zithandiza kuti  zinkazi zidzivomereza ntchito zomwe zikuchitika .

Ndipo ati ngati zitukuko ziyendetsedwa komanso kuyang`aniridwa ndi makomiti oyendetsa zitukuko m`madera, zipangitsa kuti zithu zidzichitika poyera.

A Damson ati ndikofunikira kuti khosolo yam`boma la mchinji ilimbikitse ntchito zamakomitiwa.

Padakali pano, mabugwe omwe siaboma akhala akuyenderanso ntchito zachitukuko zomwe zikuchitika pansi pa GESD m`bomali.

Zotsatira pakuyendera kuyamba , zawonetsa kuti zitukuko zina zinachitika popanda makomiti oyendetsa azachitukuko.

You may also like

Leave a Comment

Mudziwathu Community Radio Station was established in 2006 with funding from the American Institute for Research and Radio Systems Inc. It is licensed by the Malawi Regulatory Authority to serve communities in Mchinji District and surrounding areas, broadcasting on a frequency of 107.6 FM. The station’s mission is to promote socio-economic development within the district. Key focus areas include agriculture, health, gender equality, women’s empowerment, and youth development.

Newsletter

Subscribe my Newsletter for new blog posts, tips & new photos. Let's stay updated!

@2025 – All Right Reserved. MACRA Community Radios

Are you sure want to unlock this post?
Unlock left : 0
Are you sure want to cancel subscription?
-
00:00
00:00
Update Required Flash plugin
-
00:00
00:00